Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Samueli 22:22, 23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndiyeno Davide anauza Abiyatara kuti: “Tsiku lomwe lija+ nditangoona kuti Doegi wa ku Edomu aliko, ndinadziwa kuti akauza Sauli. Ineyo ndi amene ndachititsa kuti anthu onse amʼnyumba ya bambo ako aphedwe. 23 Koma iwe khala ndi ine ndipo usachite mantha. Chifukwa aliyense amene akufunafuna moyo wako akufunafunanso moyo wanga, ndipo ndikuteteza.”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani