Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Samueli 2:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Kenako ndidzasankha wansembe wanga wokhulupirika.+ Ameneyu adzachita mogwirizana ndi zimene mtima wanga ukufuna. Ndidzamʼmangira nyumba yokhalitsa, ndipo adzatumikira wodzozedwa wanga monga wansembe nthawi zonse.

  • 1 Mbiri 6:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Anthu awa anali mbadwa za Aroni:+ Aroni anabereka Eliezara,+ Eliezara anabereka Pinihasi, Pinihasi anabereka Abisuwa,

  • 1 Mbiri 6:53
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 53 Ahitubu anabereka Zadoki+ ndipo Zadoki anabereka Ahimazi.

  • 1 Mbiri 12:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Mbiri 16:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Kenako Davide anasiya Asafu+ ndi abale ake kumeneko pamaso pa likasa la pangano la Yehova, kuti azitumikira nthawi zonse kumene Likasalo linkakhala,+ mogwirizana ndi zofunika kuchita pa tsikulo.+

  • 1 Mbiri 16:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Zadoki+ wansembe ndi ansembe anzake anawasiya kuchihema cha Yehova chimene chinali pamalo okwezeka a ku Gibiyoni,+

  • 1 Mbiri 24:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani