Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mbiri 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndipo ndani angathe kumangira Mulunguyo nyumba? Chifukwa kumwamba, ngakhalenso kumwamba kwa kumwamba, nʼkosakwanira kuti akhaleko.+ Ndiye ine ndine ndani kuti ndimumangire nyumba, kupatulapo yoperekeramo nsembe pamaso pake?

  • Yesaya 40:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndi ndani anayezapo madzi onse amʼnyanja pachikhatho cha dzanja lake?+

      Ndi ndani anayezapo kumwamba ndi dzanja lake?

      Ndi ndani anasonkhanitsapo fumbi lonse lapadziko lapansi mʼmbale yoyezera+

      Kapena kuyeza mapiri pachoyezera

      Komanso zitunda pasikelo?

  • Machitidwe 17:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani