Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 10:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mfumu Solomo anapanga zishango 200 zikuluzikulu za golide wosakaniza ndi zitsulo zina.+ (Chishango chilichonse anachikuta ndi golide wolemera masekeli* 600.)+ 17 Anapanganso zishango 300 zingʼonozingʼono* za golide wosakaniza ndi zitsulo zina. (Chishango chilichonse anachikuta ndi golide wolemera ma mina* atatu.) Kenako mfumuyo inaika zishangozi mʼnyumba yotchedwa Nkhalango ya Lebanoni.+

  • 1 Mafumu 14:25-28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Mʼchaka cha 5 cha Mfumu Rehobowamu, Sisaki mfumu ya Iguputo+ anaukira Yerusalemu.+ 26 Iye anatenga chuma chamʼnyumba ya Yehova ndi chuma chamʼnyumba ya mfumu.+ Anatenga chilichonse kuphatikizapo zishango zonse zagolide zimene Solomo anapanga.+ 27 Choncho Mfumu Rehobowamu anapanga zishango zakopa* mʼmalomwake ndipo anazipereka kwa akulu a asilikali* olondera pakhomo la nyumba ya mfumu kuti aziziyangʼanira. 28 Nthawi iliyonse imene mfumuyo ikupita kunyumba ya Yehova, asilikaliwo ankanyamula zishangozo ndipo kenako ankazibwezera kuchipinda cha alonda.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani