-
Levitiko 27:30Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
30 Chakhumi chilichonse+ cha zinthu zamʼdzikolo, kaya ndi zokolola zamʼmunda kapena zipatso zamʼmitengo, ndi za Yehova. Chakhumi chimenechi ndi chopatulika kwa Yehova.
-