Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ezara 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Kenako Yesuwa+ mwana wa Yehozadaki ndi ansembe anzake ndiponso Zerubabele+ mwana wa Salatiyeli+ ndi abale ake, anakamanga guwa lansembe la Mulungu wa Isiraeli. Anachita zimenezi kuti aziperekerapo nsembe zopsereza, mogwirizana ndi zimene zinalembedwa mʼChilamulo cha Mose,+ munthu wa Mulungu woona.

  • Hagai 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndiyeno Zerubabele+ mwana wa Salatiyeli,+ Yoswa mwana wa Yehozadaki+ mkulu wa ansembe ndiponso anthu ena onse anamvera mawu a Yehova Mulungu wawo ndi a mneneri Hagai, chifukwa Yehova Mulungu wawo ndi amene anamutuma. Ndipo anthuwo anayamba kuchita mantha chifukwa cha Yehova.

  • Luka 3:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Luka 3:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani