-
Numeri 23:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Ndingathe bwanji kutemberera anthu amene Mulungu sanawatemberere?
Ndipo ndingathe bwanji kuitanira tsoka anthu amene Yehova sanawaitanire tsoka?+
-
-
Numeri 24:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Kenako Balaki anapsera mtima Balamu. Ndiyeno Balaki anawomba mʼmanja mokwiya nʼkuuza Balamu kuti: “Ndinakuitana kuti udzatemberere adani anga,+ koma iwe wawadalitsa kwambiri maulendo atatu onsewa.
-