Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Nehemiya 5:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Nehemiya 13:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mundikumbukire,+ inu Mulungu wanga, chifukwa cha zinthu zimenezi ndiponso chikondi chokhulupirika chimene ndinasonyeza chifukwa cha nyumba ya Mulungu wanga ndi zonse zochitika kumeneko.+

  • Nehemiya 13:30, 31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndiyeno ndinawayeretsa ku zinthu zonse zodetsa za anthu a mitundu ina. Komanso ndinapereka ntchito kwa ansembe ndi Alevi, aliyense ndinamʼpatsa ntchito yake.+ 31 Ndinakonzanso zoti ena azibweretsa nkhuni+ pa nthawi zoikidwiratu ndiponso mbewu zoyamba kucha.

      Inu Mulungu wanga, mundikumbukire pa zabwino zimene ndinachita.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani