Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yoswa 9:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yoswa 9:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Mbiri 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Oyamba kubwerera nʼkukakhala kucholowa chawo mʼmizinda yawo anali Aisiraeli ena, ansembe, Alevi ndi atumiki apakachisi.*+

  • Ezara 2:43-54
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Atumiki apakachisi:*+ Ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti, 44 ana a Kerosi, ana a Siyaha, ana a Padoni, 45 ana a Lebana, ana a Hagaba, ana a Akubu, 46 ana a Hagabu, ana a Salimai, ana a Hanani, 47 ana a Gideli, ana a Gahara, ana a Reyaya, 48 ana a Rezini, ana a Nekoda, ana a Gazamu, 49 ana a Uziza, ana a Paseya, ana a Besai, 50 ana a Asena, ana a Meyuni, ana a Nefusimu, 51 ana a Bakibuki, ana a Hakufa, ana a Harihuri, 52 ana a Baziluti, ana a Mehida, ana a Harisa, 53 ana a Barikosi, ana a Sisera, ana a Tema, 54 ana a Neziya ndi ana a Hatifa.

  • Ezara 8:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kenako ndinawalamula kuti apite kwa Ido yemwe anali mtsogoleri pamalo otchedwa Kasifiya. Ndinawauza mawu oti akauze Ido ndi abale ake, atumiki apakachisi* omwe anali ku Kasifiyako kuti atibweretsere atumiki apanyumba ya Mulungu wathu.

  • Ezara 8:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kuchokera pa atumiki apakachisi* amene Davide ndi akalonga anawaika kuti azitumikira Alevi, panali atumiki a pakachisi 220. Onsewa anawasankha pochita kuwatchula mayina awo.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani