Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yobu 10:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiye nʼchifukwa chiyani munanditulutsa mʼmimba mwa mayi anga?+

      Zikanakhala bwino ndikanafa diso lililonse lisanandione.

      19 Zikanakhala ngati sindinakhaleko.

      Ndikanangochokera mʼmimba nʼkupita kumanda.’

  • Yeremiya 15:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsoka ine, chifukwa inu mayi anga munabereka ine,+

      Munthu amene nthawi zonse ndimakangana ndi dziko lonse komanso kulimbana nalo.

      Sindinakongole kanthu kapena kukongoza wina aliyense,

      Koma anthu onse akunditemberera.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani