Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yobu 41:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 “Kodi ungawedze ngʼona*+ ndi mbedza

      Kapena kumanga lilime lake ndi chingwe?

  • Yobu 41:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Palibe angalimbe mtima kuti aipute.

      Ndiye ndi ndani amene angaimitsane ndi ine?+

  • Salimo 104:25, 26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Pali nyanja, yomwe ndi yakuya komanso yaikulu kwambiri,

      Mmene muli zamoyo zosawerengeka, zazikulu ndi zazingʼono zomwe.+

      26 Sitima zimayenda mmenemo,

      Ndipo Leviyatani*+ munamupanga kuti azisewera mmenemo.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani