Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 58:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Inu Mulungu, agululeni mano mʼkamwa mwawo.

      Inu Yehova, thyolani nsagwada za mikango* imeneyi.

  • Miyambo 30:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pali mʼbadwo umene mano ake ndi malupanga

      Ndiponso umene nsagwada zake ndi mipeni yophera nyama.

      Mʼbadwowo umapondereza anthu ovutika apadziko lapansi

      Komanso osauka pakati pa anthu.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani