Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ekisodo 20:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yobu 4:18-20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yobu 22:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yobu 25:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ngakhale mwezi si wowala kwa iye

      Ndipo nyenyezi si zoyera mʼmaso mwake,

       6 Ndiye kuli bwanji munthu yemwe ndi mphutsi,

      Komanso mwana wa munthu yemwe ndi nyongolotsi?”

  • Yobu 42:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tsopano utenge ngʼombe zamphongo 7 ndi nkhosa zamphongo 7. Upite nazo kwa mtumiki wanga Yobu, ndipo inuyo mukapereke nsembe yopsereza chifukwa cha tchimo lanu. Ndiyeno Yobu mtumiki wanga akakupemphererani.+ Ndithudi ineyo ndidzayankha pempho lake* kuti ndisakuchitireni zinthu mogwirizana ndi zopusa zimene mwachita, chifukwa simunanene zoona zokhudza ine ngati mmene wachitira mtumiki wanga Yobu.”

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani