-
Yobu 25:5, 6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Ngakhale mwezi si wowala kwa iye
Ndipo nyenyezi si zoyera mʼmaso mwake,
6 Ndiye kuli bwanji munthu yemwe ndi mphutsi,
Komanso mwana wa munthu yemwe ndi nyongolotsi?”
-
-
Yobu 42:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Tsopano utenge ngʼombe zamphongo 7 ndi nkhosa zamphongo 7. Upite nazo kwa mtumiki wanga Yobu, ndipo inuyo mukapereke nsembe yopsereza chifukwa cha tchimo lanu. Ndiyeno Yobu mtumiki wanga akakupemphererani.+ Ndithudi ineyo ndidzayankha pempho lake* kuti ndisakuchitireni zinthu mogwirizana ndi zopusa zimene mwachita, chifukwa simunanene zoona zokhudza ine ngati mmene wachitira mtumiki wanga Yobu.”
-