Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Mafumu 4:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mulungu anapatsa Solomo nzeru, luso lozindikira komanso mtima womvetsa zinthu zambirimbiri ngati mchenga wa mʼmbali mwa nyanja.+

  • Yobu 35:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Miyambo 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Mlaliki 2:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Munthu amene amasangalatsa Mulungu, Mulunguyo amamʼpatsa nzeru ndi kudziwa zinthu komanso amamuchititsa kuti azisangalala.+ Koma munthu wochimwa amamʼpatsa ntchito yotuta ndi kusonkhanitsa zinthu kuti azipereke kwa munthu amene amasangalatsa Mulungu woona.+ Zimenezinso nʼzachabechabe, zili ngati kuthamangitsa mphepo.

  • Danieli 1:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mulungu woona anachititsa kuti anyamata* 4 amenewa akhale odziwa zinthu komanso ozindikira zinthu zonse zolembedwa ndipo anawapatsa nzeru. Danieli anamupatsa nzeru zoti azitha kumvetsa bwino masomphenya ndi maloto amtundu uliwonse.+

  • Mateyu 11:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yakobo 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani