Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Genesis 6:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 2 Mbiri 16:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yobu 31:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Miyambo 5:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chifukwa maso a Yehova amaona chilichonse chimene munthu akuchita,

      Ndipo iye amafufuza njira zake zonse.+

  • Miyambo 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Maso a Yehova ali paliponse,

      Amaona anthu oipa ndi abwino omwe.+

  • Yeremiya 16:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Chifukwa maso anga akuona chilichonse chimene akuchita.*

      Anthuwo sanabisike kwa ine,

      Ndipo zolakwa zawo sizinabisike pamaso panga.

  • Yeremiya 32:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Zolinga zanu ndi zazikulu ndipo zochita zanu ndi zamphamvu.+ Maso anu amaona zonse zimene anthu amachita,+ kuti munthu aliyense mumuchitire zinthu mogwirizana ndi njira zake komanso zochita zake.+

  • 1 Petulo 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani