Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yobu 40:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Kodi uli ndi dzanja lamphamvu ngati la Mulungu woona?+

      Kapena kodi mawu ako angagunde ngati mabingu mofanana ndi mawu a Mulungu?+

  • Salimo 29:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mawu a Yehova akumveka pamwamba pa madzi,

      Mawu a Mulungu waulemerero akugunda ngati bingu.+

      Yehova ali pamwamba pa madzi ambiri.+

  • Salimo 68:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Imbirani iye amene wakwera pamwamba pa kumwamba,+ kumene kwakhalapo kuyambira kalekale.

      Mawu ake amphamvu amamveka ngati bingu.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani