-
Nehemiya 9:33Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
33 Inu mwachita zinthu molungama pa zonse zimene zatichitikira. Mwachita zinthu mokhulupirika koma ife ndi amene tachita zinthu zoipa.+
-
-
Salimo 59:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Koma ine, ndidzaimba za mphamvu zanu.+
Mʼmawa ndidzanena mosangalala za chikondi chanu chokhulupirika.
-
-
Danieli 9:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Inu Yehova ndinu wolungama, koma ifeyo tadzibweretsera manyazi* ngati mmene zilili lero. Manyazi agwira amuna a mu Yuda, anthu a ku Yerusalemu ndi anthu onse a ku Isiraeli, amene ali pafupi ndiponso amene ali kutali, kumayiko onse amene munawabalalitsirako chifukwa choti anakuchitirani zinthu zosakhulupirika.+
-