Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 6:10-12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yobu 31:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ngati ndikudalira golide,

      Kapena kuuza golide woyenga bwino kuti, ‘Ndimadalira iwe.’+

  • Yobu 31:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Chimenecho chikanakhala cholakwa chimene oweruza akuyenera kundipatsa chilango,

      Chifukwa ndikanakhala nditakana Mulungu woona wakumwamba.

  • Miyambo 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Miyambo 11:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Munthu amene amadalira chuma chake adzakumana ndi mavuto,+

      Koma anthu olungama adzasangalala ngati mtengo wa masamba obiriwira.+

  • Miyambo 23:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Usadzitopetse pofuna kupeza chuma.+

      Leka kuchita zimenezi, mʼmalomwake uzisonyeza kuti ndiwe womvetsa zinthu.*

       5 Ukayangʼana pamene panali chumacho, umapeza kuti palibe,+

      Chifukwa ndithu chimamera mapiko ngati chiwombankhanga nʼkuulukira mʼmwamba.+

  • Mateyu 6:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Mateyu 6:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Maliko 8:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Luka 12:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Timoteyo 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Yohane 2:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani