- 
	                        
            
            Yesaya 50:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
 - 
                            
- 
                                        
6 Msana wanga ndinaupereka kwa anthu amene ankandimenya
Ndipo masaya anga ndinawapereka kwa anthu amene ankandizula ndevu.
Sindinabise nkhope yanga kuti asaichitire zinthu zochititsa manyazi komanso kuti asailavulire.+
 
 -