Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 10:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 10:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mumtima mwake amanena kuti: “Mulungu waiwala zoipa zimene ndimachita.+

      Iye wayangʼana kumbali.

      Sakuona chilichonse.”+

  • Salimo 94:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, kodi anthu oipa adzapitiriza kusangalala mpaka liti?

      Adzapitiriza kukondwera mpaka liti?+

  • Salimo 94:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iwo amanena kuti: “Ya sakuona,+

      Ndipo Mulungu wa Yakobo sakudziwa zimene zikuchitika.”+

  • Ezekieli 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iye anandiuza kuti: “Iwe mwana wa munthu, kodi waona zimene akuluakulu a Isiraeli akuchita mumdima? Kodi waona zimene aliyense wa iwo akuchita mʼzipinda zake zamkati mmene muli mafano ake? Iwo akunena kuti, ‘Yehova sakutiona. Yehova wachokamo mʼdziko muno.’”+

  • Zefaniya 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa nthawi imeneyo ndidzafufuza ndi nyale mosamala kwambiri mu Yerusalemu,

      Ndipo ndidzaweruza anthu amene akukhala mosatekeseka* nʼkumaganiza kuti,

      ‘Yehova sadzachita zabwino kapena zoipa.’+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani