Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 31:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Msuri adzaphedwa ndi lupanga, koma osati la munthu.

      Lupanga lidzamudya, koma osati la munthu.+

      Iye adzathawa chifukwa cha lupangalo

      Ndipo anyamata ake adzagwiritsidwa ntchito yaukapolo.

  • Yesaya 37:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ndiyeno mngelo wa Yehova anapita kumsasa wa Asuri nʼkukapha asilikali 185,000. Anthu podzuka mʼmawa, anangoona kuti onse ndi mitembo yokhayokha.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani