Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Samueli 10:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Patapita nthawi, Aamoni anaona kuti akhala ngati chinthu chonunkha kwa Davide. Choncho anatumiza anthu kuti akalembe ganyu Asiriya a ku Beti-rehobu+ ndi Asiriya a ku Zoba+ ndipo onse pamodzi analipo asilikali 20,000 oyenda pansi. Anapitanso kwa mfumu ya ku Maaka+ nʼkulemba ganyu amuna 1,000 komanso ku Isitobu amuna 12,000.+

  • Yesaya 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno kunyumba ya Davide kunapita uthenga wakuti: “Dziko la Siriya lachita mgwirizano ndi dziko la Efuraimu.”

      Choncho mtima wa Ahazi ndi wa anthu ake unayamba kunjenjemera, ngati mitengo ya mʼnkhalango imene ikugwedezeka ndi mphepo.

  • Yesaya 7:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Chifukwa Siriya ndi Efuraimu ndiponso mwana wa Remaliya akukonzera zoipa ndipo anena kuti:

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani