- 
	                        
            
            Mika 7:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        9 Ndidzapirira mkwiyo wa Yehova, Chifukwa ndamuchimwira.+ Ndidzaupirira mpaka ataweruza mlandu wanga nʼkundichitira chilungamo. Iye adzandipititsa pamalo owala, Ndipo ndidzaona chilungamo chake. 
 
-