Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 112:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Kwa anthu owongoka mtima iye amawala ngati kuwala kumene kumaunika mumdima.+

      ח [Heth]

      Iye ndi wokoma mtima,* wachifundo+ komanso wolungama.

  • Miyambo 4:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 30:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Mika 7:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Ndidzapirira mkwiyo wa Yehova,

      Chifukwa ndamuchimwira.+

      Ndidzaupirira mpaka ataweruza mlandu wanga nʼkundichitira chilungamo.

      Iye adzandipititsa pamalo owala,

      Ndipo ndidzaona chilungamo chake.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani