- 
	                        
            
            2 Mafumu 21:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        16 Manase anaphanso anthu ambiri osalakwa mpaka magazi awo anadzaza Yerusalemu kuyambira koyambirira mpaka kumapeto,+ kuwonjezera pa tchimo lake lochititsa kuti Ayuda achimwe pochita zoipa pamaso pa Yehova. 
 
-