Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 38:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 103:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 143:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 143 Inu Yehova, imvani pemphero langa.+

      Mvetserani kuchonderera kwanga kopempha thandizo.

      Ndiyankheni mogwirizana ndi kukhulupirika kwanu komanso chilungamo chanu.

       2 Musandiimbe mlandu ine mtumiki wanu,

      Chifukwa palibe aliyense wamoyo amene angakhale wolungama pamaso panu.+

  • Yesaya 55:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Danieli 9:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Inu Mulungu wanga, tcherani khutu lanu kuti mumve. Tsegulani maso anu kuti muone zimene zatichitikira komanso mmene mzinda wodziwika ndi dzina lanu wawonongekera. Ifeyo sitikukuchondererani chifukwa choti tachita zinthu zolungama ayi, koma chifukwa cha chifundo chanu chachikulu.+

  • Aroma 3:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Tito 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani