Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mbiri 16:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Pa nthawi imodzimodziyo mitengo yamʼnkhalango ifuule mosangalala pamaso pa Yehova,

      Chifukwa iye akubwera* kudzaweruza dziko lapansi.

  • Yesaya 44:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Fuulani mosangalala kumwamba inu,

      Chifukwa Yehova wachita zimenezi.

      Fuulani posonyeza kupambana, inu malo otsika kwambiri a dziko lapansi.

      Mapiri inu, fuulani mosangalala,+

      Iwe nkhalango ndi inu mitengo yonse imene ili mmenemo,

      Chifukwa Yehova wawombola Yakobo,

      Ndipo wasonyeza kukongola kwake pa Isiraeli.”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani