Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 31:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 79:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 109:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Koma inu, Yehova Ambuye Wamkulu Koposa,

      Ndithandizeni kuti dzina lanu lilemekezedwe.+

      Ndipulumutseni chifukwa chikondi chanu chokhulupirika nʼchabwino.+

  • Salimo 143:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inu Yehova, ndithandizeni kuti ndikhalebe ndi moyo chifukwa cha dzina lanu.

      Ndipulumutseni mʼmavuto anga, chifukwa ndinu wachilungamo.+

  • Ezekieli 36:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 “Choncho uza nyumba ya Isiraeli kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Sindidzachita zimenezi chifukwa cha inuyo a nyumba ya Isiraeli, koma chifukwa cha dzina langa loyera limene munalidetsa pakati pa anthu a mitundu ina kumene munapita.”’+

  • Danieli 9:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Imvani, inu Yehova. Tikhululukireni,+ inu Yehova. Timvereni ndipo muchitepo kanthu, inu Yehova! Musazengereze inu Mulungu wanga, chifukwa cha dzina lanu. Chifukwa mzinda wanu ndi anthu anu amadziwika ndi dzina lanu.”+

  • Mateyu 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani