Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 9:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Esitere 1:10-12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pa tsiku la 7, mtima wa mfumu utasangalala chifukwa chomwa vinyo, mfumuyo inauza Mehumani, Bizita, Haribona,+ Bigita, Abagata, Zetara ndi Karikasi, nduna 7 zomwe zinkatumikira Mfumu Ahasiwero, 11 kuti akatenge Mfumukazi Vasiti nʼkubwera naye kwa mfumu atavala duku lachifumu, kuti anthu onse ndi akalonga aone kukongola kwake, chifukwa analidi wokongola kwambiri. 12 Koma Mfumukazi Vasiti anakana atauzidwa ndi nduna zapanyumba ya mfumu kuti mfumu yalamula kuti apite. Zitatero mfumuyo inakwiya kwambiri ndipo inapsa mtima.

  • Miyambo 6:25, 26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Usasirire kukongola kwake mumtima mwako.+

      Kapena kulola kuti ukopeke ndi maso ake achikoka,

      26 Munthu amafika potsala ndi mkate umodzi wokha chifukwa cha hule,+

      Koma mkazi wa mwini amasaka moyo wako wamtengo wapatali.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani