Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Genesis 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yobu 27:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Ngati ndikupitirizabe kupuma,

      Ndiponso mzimu wochokera kwa Mulungu uli mʼmphuno mwanga,+

  • Yobu 34:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iye akakwiyira anthu,

      Nʼkutenga mphamvu ya moyo* komanso mpweya wawo,+

      15 Anthu onse amafera limodzi,

      Ndipo anthuwo amabwerera kufumbi.+

  • Salimo 104:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mukabisa nkhope yanu, zimasokonezeka.

      Mukachotsa mzimu wawo,* zimafa ndipo zimabwerera kufumbi.+

  • Yesaya 42:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mulungu woona Yehova,

      Amene analenga kumwamba ndiponso Mulungu Wamkulu amene anakutambasula,+

      Amene anapanga dziko lapansi ndi zonse zimene zili mmenemo,+

      Amene amapereka mpweya kwa anthu amene ali mmenemo,+

      Komanso mzimu* kwa anthu amene amayenda padzikolo,+ wanena kuti:

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani