Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Mlaliki 2:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Chifukwa munthu wanzeru komanso munthu wopusa,+ onsewa sadzakumbukiridwa mpaka kalekale. Mʼmasiku amene akubwerawa aliyense adzaiwalika. Ndipo kodi wanzeru adzafa bwanji? Adzafa mofanana ndi wopusa.+

  • Mlaliki 9:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 40:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Tamvera! Winawake akunena kuti: “Lengeza mofuula!”

      Wina akufunsa kuti: “Ndilengeze mofuula za chiyani?”

      “Anthu onse ali ngati udzu wobiriwira.

      Chikondi chawo chonse chokhulupirika chili ngati duwa lakutchire.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani