-
1 Mafumu 9:22Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
22 Koma palibe Aisiraeli amene Solomo anawasandutsa akapolo,+ chifukwa iwo anali asilikali ake, atumiki ake, akalonga ake, asilikali othandiza pa magaleta ndiponso atsogoleri a asilikali ake oyendetsa magaleta ndi amuna okwera pamahatchi.
-