Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Nyimbo ya Solomo 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 “Undikise ndi milomo yako,

      Chifukwa chikondi chimene umandisonyeza chimaposa vinyo.+

  • Nyimbo ya Solomo 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Nditenge, tiye tithawe.

      Chifukwatu mfumu yandipititsa mʼzipinda zake zamkati.

      Tiye tikondwere komanso kusangalalira limodzi.

      Tiye titamande* chikondi chimene umandisonyeza kuposa kutamanda vinyo.

      Mpake kuti atsikana amakukonda.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani