Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 44:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Munthu wosula zitsulo akugwiritsa ntchito chida chake posula chitsulo chimene wachiwotcha pamoto wamakala.

      Akuchiwongola ndi hamala,

      Akuchisula ndi dzanja lake lamphamvu.+

      Kenako wamva njala ndipo mphamvu zake zatha.

      Sanamwe madzi ndipo watopa.

  • Yesaya 46:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pali anthu amene amakhuthula golide mʼzikwama zawo.

      Amayeza siliva pasikelo.

      Iwo amalemba ganyu mmisiri wa zitsulo ndipo amapanga mulungu ndi zinthu zimenezi.+

      Kenako anthuwo amayamba kumuweramira ndi kumulambira.*+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani