Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 60:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Dzuwa silidzakhalanso lokuunikira masana,

      Ndipo mwezi sudzakuunikiranso.

      Chifukwa Yehova adzakhala kuwala kwako mpaka kalekale,+

      Ndipo Mulungu wako adzakhala kukongola kwako.+

      20 Dzuwa lako silidzalowanso,

      Ndipo mwezi wako sudzasiya kuwala,

      Chifukwa Yehova adzakhala kuwala kwako mpaka kalekale,+

      Ndipo masiku ako olira adzakhala atatha.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani