-
2 Mbiri 36:22, 23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
22 Mʼchaka choyamba cha Koresi+ mfumu ya Perisiya, pokwaniritsa mawu a Yehova amene analankhula kudzera mwa Yeremiya,+ Yehova analimbikitsa Koresi mfumu ya Perisiya kuti alengeze mu ufumu wake wonse, zomwenso iye analemba mʼmakalata,+ kuti: 23 “Koresi mfumu ya Perisiya wanena kuti, ‘Yehova Mulungu wakumwamba wandipatsa maufumu onse apadziko lapansi.+ Iye wandituma kuti ndimumangire nyumba ku Yerusalemu mʼdziko la Yuda.+ Aliyense amene ali pakati panu mwa anthu onse amene amamutumikira, Yehova Mulungu wake akhale naye ndipo apite.’”+
-
-
Yesaya 45:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 Ine ndapatsa munthu mphamvu kuti achitepo kanthu mwachilungamo,+
Ndipo njira zake zonse ndidzaziwongola.
-