-
Yeremiya 51:29Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
29 Dziko lidzagwedezeka ndi kunjenjemera,
Chifukwa Yehova adzachitira Babulo zimene akuganiza
Kuti dziko la Babulo likhale chinthu chochititsa mantha, lopanda munthu wokhalamo.+
-