-
Yesaya 44:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Fuulani mosangalala kumwamba inu,
Chifukwa Yehova wachita zimenezi.
Fuulani posonyeza kupambana, inu malo otsika kwambiri a dziko lapansi.
Mapiri inu, fuulani mosangalala,+
Iwe nkhalango ndi inu mitengo yonse imene ili mmenemo,
Chifukwa Yehova wawombola Yakobo,
Ndipo wasonyeza kukongola kwake pa Isiraeli.”+
-
-
Yesaya 61:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Kuti ndisamalire anthu onse amene akulirira Ziyoni,
Kuti ndiwapatse nsalu yovala kumutu mʼmalo mwa phulusa,
Kuti ndiwapatse mafuta kuti azisangalala mʼmalo molira,
Kuti ndiwapatse chovala choti azivala ponditamanda mʼmalo mokhala otaya mtima.
-