Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 60:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Alendo adzamanga mipanda yako,

      Ndipo mafumu awo adzakutumikira.+

      Ine ndinakulanga chifukwa ndinali nditakwiya,

      Koma chifukwa cha kukoma mtima kwanga* ndidzakuchitira chifundo.+

  • Yesaya 60:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Iwe udzamwa mkaka wa mitundu ya anthu,+

      Ndipo udzayamwa bere la mafumu.+

      Udzadziwadi kuti ine Yehova ndine Mpulumutsi wako,

      Ndiponso kuti Wamphamvu wa Yakobo ndi Wokuwombola.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani