Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Mika 7:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Anthu a mitundu ina adzaona zodabwitsazo ndipo adzachita manyazi ngakhale kuti ndi amphamvu.+

      Iwo adzagwira pakamwa,

      Ndipo makutu awo adzagontha.

      17 Adzanyambita fumbi ngati njoka.+

      Ngati nyama zokwawa, adzatuluka akunjenjemera mʼmalo awo obisalamo.

      Adzabwera kwa Yehova Mulungu akuchita mantha,

      Ndipo adzayamba kukuopani.”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani