Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 29:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndidzakulolani kuti mundipeze,’+ akutero Yehova. ‘Ndidzasonkhanitsa anthu amene anagwidwa nʼkutengedwa kupita kumayiko ena kuchokera mʼmitundu yonse ndi kumalo onse kumene ndinakubalalitsirani,’+ akutero Yehova. ‘Kenako ndidzakubwezeretsani kumalo amene ndinakuchotsani pa nthawi imene ndinakupititsani ku ukapolo.’+

  • Yeremiya 46:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 ‘Koma iwe Yakobo mtumiki wanga, usaope

      Ndipo usachite mantha, iwe Isiraeli.+

      Chifukwa ndidzakupulumutsa kuchokera kutali.

      Ndipo ndidzapulumutsa mbadwa* yako kuchokera mʼdziko limene anali kapolo.+

      Yakobo adzabwerera nʼkukhala mwamtendere ndiponso mosatekeseka,

      Sipadzakhala wowaopseza.+

  • Hoseya 6:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Komanso, inu anthu a ku Yuda, nthawi yoti mukololedwe yakhazikitsidwa.

      Ine ndidzasonkhanitsanso anthu anga amene anatengedwa kupita kudziko lina.”+

  • Yoweli 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani