Yesaya 44:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Ndine amene ndimachititsa mawu a mtumiki wanga kuti akwaniritsidweNdiponso amene ndimakwaniritsa mawu onse amene amithenga anga analosera.+Ndine amene ndikunena za Yerusalemu kuti, ‘Muzidzakhala anthu.’+ Ndikunenanso za mizinda ya ku Yuda kuti, ‘Idzamangidwanso,+Ndipo ndidzakonza malo ake amene anawonongedwa.’+ Yesaya 61:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Iwo adzamanganso malo amene akhala bwinja kwa nthawi yaitali.Adzamanga malo amene anasakazidwa kalekale,+Adzakonzanso mizinda imene inawonongedwa,+Malo amene akhala ali osakazidwa kumibadwomibadwo.+
26 Ndine amene ndimachititsa mawu a mtumiki wanga kuti akwaniritsidweNdiponso amene ndimakwaniritsa mawu onse amene amithenga anga analosera.+Ndine amene ndikunena za Yerusalemu kuti, ‘Muzidzakhala anthu.’+ Ndikunenanso za mizinda ya ku Yuda kuti, ‘Idzamangidwanso,+Ndipo ndidzakonza malo ake amene anawonongedwa.’+ Yesaya 61:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Iwo adzamanganso malo amene akhala bwinja kwa nthawi yaitali.Adzamanga malo amene anasakazidwa kalekale,+Adzakonzanso mizinda imene inawonongedwa,+Malo amene akhala ali osakazidwa kumibadwomibadwo.+
4 Iwo adzamanganso malo amene akhala bwinja kwa nthawi yaitali.Adzamanga malo amene anasakazidwa kalekale,+Adzakonzanso mizinda imene inawonongedwa,+Malo amene akhala ali osakazidwa kumibadwomibadwo.+