Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ezara 1:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 48:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tulukani mʼBabulo!+

      Thawani mʼmanja mwa Akasidi.

      Lengezani zimenezi mofuula komanso mosangalala. Uzani anthu zimenezi.+

      Zineneni kuti anthu azidziwe mpaka kumalekezero a dziko lapansi.+

      Munene kuti: “Yehova wawombola mtumiki wake Yakobo.+

  • Yesaya 52:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iwe Yerusalemu dzuka, sansa fumbi ndipo ukhale pampando.

      Masula zingwe zimene zili mʼkhosi mwako, iwe mwana wamkazi wa Ziyoni* amene unagwidwa nʼkutengedwa kupita kudziko lina.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani