Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 22:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Anthu onse ochokera kumalekezero a dziko lapansi adzakumbukira Yehova nʼkupita kwa iye.

      Ndipo mabanja onse a mitundu ya anthu adzagwada pamaso panu.+

  • Yesaya 49:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ndiyeno iye anati: “Sikuti wangokhala mtumiki wanga

      Kuti ubwezeretse mafuko a Yakobo

      Ndiponso kuti Aisiraeli amene ali otetezeka uwabwezere kwawo.

      Koma ndakuperekanso kuti ukhale kuwala kwa anthu a mitundu ina,+

      Kuti chipulumutso changa chifike kumalekezero a dziko lapansi.”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani