Deuteronomo 30:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Yehova Mulungu wanu adzabweza kwawo anthu a mtundu wanu amene anagwidwa nʼkupita kudziko lina,+ ndipo adzakuchitirani chifundo+ nʼkukusonkhanitsaninso pamodzi kuchokera pakati pa anthu onse kumene Yehova Mulungu wanu anakubalalitsirani.+ Yesaya 27:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Pa tsiku limenelo Yehova adzathyola zipatso kuchokera ku Mtsinje* mpaka kukafika kukhwawa la Iguputo+ ndipo mudzasonkhanitsidwa mmodzimmodzi, inu Aisiraeli.+ Hoseya 1:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ayuda ndi Aisiraeli adzasonkhanitsidwa pamodzi ndipo adzakhala ogwirizana.+ Iwo adzasankha mtsogoleri mmodzi nʼkutuluka mʼdzikolo chifukwa tsiku limeneli lidzakhala lofunika kwambiri kwa Yezereeli.”+
3 Yehova Mulungu wanu adzabweza kwawo anthu a mtundu wanu amene anagwidwa nʼkupita kudziko lina,+ ndipo adzakuchitirani chifundo+ nʼkukusonkhanitsaninso pamodzi kuchokera pakati pa anthu onse kumene Yehova Mulungu wanu anakubalalitsirani.+
12 Pa tsiku limenelo Yehova adzathyola zipatso kuchokera ku Mtsinje* mpaka kukafika kukhwawa la Iguputo+ ndipo mudzasonkhanitsidwa mmodzimmodzi, inu Aisiraeli.+
11 Ayuda ndi Aisiraeli adzasonkhanitsidwa pamodzi ndipo adzakhala ogwirizana.+ Iwo adzasankha mtsogoleri mmodzi nʼkutuluka mʼdzikolo chifukwa tsiku limeneli lidzakhala lofunika kwambiri kwa Yezereeli.”+