-
Yesaya 62:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Taonani! Yehova walengeza mpaka kumalekezero a dziko lapansi kuti:
Taona! Mphoto yake ili ndi iyeyo,
Ndipo malipiro amene amapereka ali pamaso pake.’”+
-