Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 60:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Anthu ako onse adzakhala olungama.

      Adzatenga dzikoli kukhala lawo mpaka kalekale.

      Anthuwo ndi mmera umene ndinadzala,

      Ndiponso ntchito ya manja anga,+ kuti ineyo ndioneke kukongola.+

  • Ezekieli 37:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiye uwauze kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Ine nditenga Aisiraeli kuchokera kwa anthu a mitundu ina kumene anapita. Ndidzawasonkhanitsa pamodzi kuchokera kumbali zonse ndipo ndidzawabweretsa mʼdziko lawo.+

  • Obadiya 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Anthu onse opulumuka adzakhala paphiri la Ziyoni+

      Ndipo phiri limeneli lidzakhala loyera.+

      Anthu a mʼbanja la Yakobo adzatenganso zinthu zimene zinali zawo.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani