Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 15:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mʼmasiku a Peka mfumu ya Isiraeli, Tigilati-pilesere+ mfumu ya Asuri anabwera nʼkulanda Iyoni, Abele-beti-maaka,+ Yanoa, Kedesi,+ Hazori, Giliyadi+ ndi Galileya, dera lonse la Nafitali.+ Anatenga anthu akumeneku nʼkupita nawo ku Asuri.+

  • 2 Mafumu 16:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako Ahazi anatenga siliva ndi golide wapanyumba ya Yehova ndiponso wochokera mʼnyumba ya mfumu nʼkutumiza kwa mfumu ya Asuri ngati chiphuphu.+ 9 Mfumu ya Asuri inamvera pempho lake ndipo inapita ku Damasiko nʼkukalanda mzindawo. Anthu amumzindawo inawagwira nʼkupita nawo ku Kiri+ ndipo Rezini inamupha.+

  • 2 Mafumu 17:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 7:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mwanayo asanafike podziwa kukana choipa ndi kusankha chabwino, mayiko a mafumu awiri amene ukuchita nawo manthawo, adzakhala atasiyidwiratu.+

  • Yesaya 17:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Uwu ndi uthenga wokhudza Damasiko:+

      “Taonani! Damasiko sadzakhalanso mzinda,

      Adzawonongedwa nʼkukhala mabwinja okhaokha.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani