Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 60:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mitundu ya anthu idzatsata kuwala kwako,+

      Ndipo mafumu+ adzatsata ulemerero wako wonyezimira.*+

  • Malaki 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Kuchokera kotulukira dzuwa kukafika kumene limalowera,* dzina langa lidzakwezeka pakati pa anthu a mitundu ina.+ Kulikonse anthu azidzapereka nsembe zautsi ndiponso nsembe zina ngati mphatso zovomerezeka polemekeza dzina langa. Adzachita izi chifukwa dzina langa lidzakwezeka pakati pa anthu a mitundu inawo,”+ watero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani