Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Amosi 2:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Amapondaponda mitu ya anthu wamba pafumbi,+

      Ndipo amatsekereza njira ya anthu ofatsa.+

      Bambo ndi mwana wake wamwamuna akugona ndi mtsikana mmodzi,

      Ndipo akuipitsa dzina langa loyera.

       8 Zovala zimene alanda anthu ena monga chikole,+ amaziyala pafupi ndi guwa lililonse lansembe+ nʼkugonapo.

      Ndipo vinyo amene amakamwera kunyumba* za milungu yawo, amagula ndi ndalama zimene alipiritsa anthu.’

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani