Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 9:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 30:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Taonani! Dzina la Yehova likubwera kuchokera kutali.

      Likubwera ndi mkwiyo wake woyaka moto ndiponso mitambo yolemera.

      Iye akulankhula mwaukali,

      Ndipo lilime lake lili ngati moto wowononga.+

  • Yesaya 31:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Msuri adzaphedwa ndi lupanga, koma osati la munthu.

      Lupanga lidzamudya, koma osati la munthu.+

      Iye adzathawa chifukwa cha lupangalo

      Ndipo anyamata ake adzagwiritsidwa ntchito yaukapolo.

       9 Thanthwe lake lidzachoka chifukwa cha mantha,

      Ndipo akalonga ake adzachita mantha chifukwa cha chizindikiro,” akutero Yehova,

      Amene kuwala kwake kuli mu Ziyoni* ndiponso amene ngʼanjo yake ili mu Yerusalemu.

  • Nahumu 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Iye atapsa mtima, ndani angaime pamaso pake?+

      Iye atakwiya, ndani angalimbe mtima kuima pamaso pake?+

      Mkwiyo wake adzaukhuthula ngati moto,

      Ndipo miyala idzaphwanyidwa chifukwa cha iye.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani